Baibulo ndi buku lopatulika lomwe limakhulupiliwa kuti linapatsidwa kwa anthu kuchokera kwa Mulungu. Ilo lagawidwa muzigawo ziwiri- malemba a Chiheberi ndi malemba a Chigriki. Mabukhu amene amagwiritsidwa ntchito ku Chiyuda amatchedwa Tanaka kapena Baibulo la Chiyunda. Mabukhu amene amagwiritsidwa ntchito mu Chikhristu amatcheda Bukhu Loyera, Mau a Mulungu kapena Baibulo la chi Khristu. Chikhristu chimatenga ma bukhu ena a Baibulo la Chiyuda ku Chipangano cha kale, ngakhale ma bukhu awa amasiyana pa dongosolo lake ndipo ma baibulo ena ali ndi mabukhu owonjezera. baibulo la Chikhristu lili ndi mbali ina ya chiwiri yotchedwa Chipangano cha Tsopano.

Baibulo

Mabukhu a Baibulo Sinthani

Ma bukhu a baibulo amayalidwa mofanana mu zitanthauziro zosiyana siyana. Baibulo la Chikhristu linagawidwa mbali ziwili: Chipangano cha Kale ndi Chipangano cha Tsopano.

Chipangano cha Kale Sinthani

Genesis Sinthani

Ekesodo Sinthani

20

Numeri Sinthani

Deuteronomo Sinthani

Yoswa Sinthani

Oweruza Sinthani

Rute Sinthani

1 Samueli Sinthani

2 Samueli Sinthani

1 Mafumu Sinthani

2 Mafumu Sinthani

1 Mbiri Sinthani

2 Mbiri Sinthani

Ezara Sinthani

Nehemiya Sinthani

Estere Sinthani

Yobu Sinthani

Masalimo Sinthani

Miyambo Sinthani

Mlaliki Sinthani

Nyimbo ya Solomo Sinthani

Yesaya Sinthani

Yeremiya Sinthani

Maliro Sinthani

Ezekieli Sinthani

Danieli Sinthani

Hoseya Sinthani

Yoweri Sinthani

Obadiya Sinthani

Yona Sinthani

Mika Sinthani

Nahamu Sinthani

Habakuku Sinthani

Zefaniya Sinthani

Hagai Sinthani

Zekariya Sinthani

Malaki Sinthani

Chipangano cha Tsopano Sinthani

Mateyu Sinthani

Maliko Sinthani

Luka Sinthani

Yohane Sinthani

Machitidwe a Atumwi Sinthani

Aroma Sinthani

1 Akorinto Sinthani

2 Akorinto Sinthani

Afilipi Sinthani

Akolose Sinthani

1 Atesalonika Sinthani

2 Atesalonika Sinthani

1 Timoteyo Sinthani

2 Timoteyo Sinthani

Tito Sinthani

Ahebri Sinthani

Yakobo Sinthani

1 Petro Sinthani

2 Petro Sinthani

1 Yohane Sinthani

2 Yohane Sinthani

3 Yohane Sinthani

Yuda Sinthani

Chibvumbulutso Sinthani